Masalimo 77:6 - Buku Lopatulika6 Ndikumbukira nyimbo yanga usiku; ndilingalira mumtima mwanga; mzimu wanga unasanthula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndikumbukira nyimbo yanga usiku; ndilingalira mumtima mwanga; mzimu wanga unasanthula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndimasinkhasinkha mumtima mwanga usiku. Ndimadzifunsa ndi kufufuzafufuza mumtima mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndinakumbukira nyimbo zanga usiku. Mtima wanga unasinkhasinkha ndipo mzimu wanga unafunsa kuti, Onani mutuwo |