Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 77:5 - Buku Lopatulika

5 Ndinaganizira masiku akale, zaka zakalekale.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndinaganizira masiku akale, zaka zakalekale.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndimalingalira za masiku akale, ndimakumbukira zaka zamakedzana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndinaganizira za masiku akale, zaka zamakedzana;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 77:5
8 Mawu Ofanana  

Adani anga anditonza tsiku lonse; akundiyalukirawo alumbirira ine.


Ndikumbukira masiku a kale lomwe; zija mudazichita ndilingirirapo; ndikamba pandekha za ntchito ya manja anu.


Mulungu, tidamva m'makutu mwathu, makolo athu anatisimbira, za ntchitoyo mudaichita masiku ao, masiku akale.


Galamuka, galamuka, khala ndi mphamvu, mkono wa Yehova; galamuka monga masiku akale, mibadwo ya nthawi zakale. Kodi si ndiwe amene unadula Rahabu zipinjirizipinjiri; amene unapyoza chinjoka chamnyanja chija?


Kumbukirani masiku akale, zindikirani zaka za mibadwo yambiri; funsani atate wanu, adzakufotokozerani; akulu anu, adzakuuzani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa