Masalimo 142:3 - Buku Lopatulika3 Pamene mzimu wanga unakomoka m'kati mwanga, munadziwa njira yanga. M'njira ndiyendamo ananditchera msampha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamene mzimu wanga unakomoka m'kati mwanga, munadziwa njira yanga. M'njira ndiyendamo ananditchera msampha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamene mtima wanga ufooka, Inu mumadziŵa zoti ndichite. Adani anditchera msampha m'njira imene ndimayendamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene mzimu wanga walefuka mʼkati mwanga, ndinu amene mudziwa njira yanga. Mʼnjira imene ndimayendamo anthu anditchera msampha mobisa. Onani mutuwo |