Masalimo 142:2 - Buku Lopatulika2 Nditsanulira kudandaula kwanga pamaso pake; ndionetsa msauko wanga pamaso pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nditsanulira kudandaula kwanga pamaso pake; ndionetsa msauko wanga pamaso pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndikupereka madandaulo anga kwa Iye, ndikutchula mavuto anga pamaso pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndikukhuthula madandawulo anga pamaso pake; ndikufotokoza za masautso anga pamaso pake. Onani mutuwo |