Masalimo 142:1 - Buku Lopatulika1 Ndifuula nalo liu langa kwa Yehova; ndi mau anga ndipemba kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndifuula nalo liu langa kwa Yehova; ndi mau anga ndipemba kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndikulirira Chauta mokweza, ndikupemba kwa Chauta mofuula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndikulirira Yehova mofuwula; ndikukweza mawu anga kwa Yehova kupempha chifundo. Onani mutuwo |