Masalimo 77:3 - Buku Lopatulika3 Ndikumbukira Mulungu ndipo ndivutika; ndilingalira ndipo mzimu wanga ukomoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndikumbukira Mulungu ndipo ndivutika; ndilingalira ndipo mzimu wanga ukomoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndikamalingalira za Mulungu, ndimangobuula mumtima. Ndikamasinkhasinkha za Iye, ndimataya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndinakumbukira Inu Mulungu, ndipo ndinabuwula; ndinasinkhasinkha ndipo mzimu wanga unalefuka. Sela Onani mutuwo |