Masalimo 77:2 - Buku Lopatulika2 Tsiku la nsautso yanga ndinafuna Ambuye. Dzanja langa linatambalika usiku, losaleka; mtima wanga unakana kutonthozedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Tsiku la nsautso yanga ndinafuna Ambuye. Dzanja langa linatambalika usiku, losaleka; mtima wanga unakana kutonthozedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pa tsiku lamavuto ndimafunafuna Ambuye. Usiku wonse ndimakweza manja anga ndi kupemphera kosalekeza. Mtima wanga umakana kuusangalatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pamene ndinali pa masautso ndinafunafuna Ambuye; usiku ndinatambasula manja mosalekeza ndipo moyo wanga unakana kutonthozedwa. Onani mutuwo |