Masalimo 25:16 - Buku Lopatulika16 Cheukirani ine ndipo ndichitireni chifundo; pakuti ndili wounguluma ndi wozunzika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Cheukirani ine ndipo ndichitireni chifundo; pakuti ndili wounguluma ndi wozunzika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Inu Chauta yang'aneni ine, ndipo mundikomere mtima, pakuti ndili ndekhandekha, ndipo ndazunzika kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tembenukirani kwa ine ndipo mundikomere mtima, pakuti ndili ndekhandekha ndipo ndikuzunzika. Onani mutuwo |