Masalimo 124:4 - Buku Lopatulika4 Akadatimiza madziwo, mtsinje ukadapita pa moyo wathu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Akadatimiza madziwo, mtsinje ukadapita pa moyo wathu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 bwenzi chigumula chitatisesa, madzi amkokomo atatikokolola, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 chigumula chikanatimiza, mtsinje ukanatikokolola, Onani mutuwo |
Ndipo atapita masabata makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri wodzozedwayo adzalikhidwa, nadzakhala wopanda kanthu; ndi anthu a kalonga wakudzayo adzaononga mzinda ndi malo opatulika; ndi kutsiriza kwake kudzakhala kwa chigumula, ndi kufikira chimaliziro kudzakhala nkhondo; chipasuko chalembedweratu.