Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 124:5 - Buku Lopatulika

5 madzi odzikuza akadapita pa moyo wathu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 madzi odzikuza akadapita pa moyo wathu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 bwenzi madzi amphamvu atatimiza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 madzi a mkokomo akanatikokolola.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 124:5
3 Mawu Ofanana  

ndi kuti, Ufike mpaka apa, osapitirirapo; apa adzaletseka mafunde ako odzikuza?


Kodi simundiopa Ine? Ati Yehova: simudzanthunthumira pamaso pa Ine, amene ndinaika mchenga chilekaniro cha nyanja, ndi lemba lamuyaya kuti isapitirirepo? Ndipo ngakhale mafunde ake achita gavigavi, alephera; ngakhale akokoma, sangathe kupitirirapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa