Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 47:3 - Buku Lopatulika

Atigonjetsera anthu, naika amitundu pansi pa mapazi athu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Atigonjetsera anthu, naika amitundu pansi pa mapazi athu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iye adatigonjetsera anthu ambirimbiri, mitundu ina ya anthu adaiika pansi pa ulamuliro wathu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu; anayika anthu pansi pa mapazi athu.

Onani mutuwo



Masalimo 47:3
14 Mawu Ofanana  

Yehova ananena kwa Ambuye wanga, Khalani padzanja lamanja langa, kufikira nditaika adani anu chopondapo mapazi anu.


Ndiye Mulungu amene andibwezerera chilango, nandigonjetsera mitundu ya anthu.


Idzani, muone ntchito za Mulungu; zochitira Iye ana a anthu nzoopsa.


Ndikadagonjetsa adani ao msanga, ndikadabweza dzanja langa pa owasautsa.


Pakuti Yehova ndiye Mulungu wamkulu; ndi mfumu yaikulu yoposa milungu yonse.


Yehova ndiye wamkulu mu Ziyoni; ndipo akwezeka pamwamba pa mitundu yonse ya anthu.


Wosaopa Inu ndani, Mfumu ya amitundu? Pakuti kukuopani ndi kwanu; pakuti mwa anzeru onse a amitundu, ndi m'maufumu ao onse, mulibe akunga Inu.


Ndipo Yehova adzakhala mfumu ya dziko lonse; tsiku lomwelo Yehova adzakhala Iye yekha, ndi dzina lake ilo lokha.


Koma wotembereredwa wonyengayo, wokhala nayo yaimuna m'gulu lake, nawinda, naphera Yehova nsembe chinthu chachilema; pakuti Ine ndine mfumu yaikulu, ati Yehova wa makamu; ndipo dzina langa ndi loopsa pakati pa amitundu.


Pakuti ayenera kuchita ufumu kufikira ataika adani onse pansi pa mapazi ake.


Wodala iwe, Israele; akunga iwe ndani, mtundu wa anthu opulumutsidwa ndi Yehova, ndiye chikopa cha thandizo lako, Iye amene akhala lupanga la ukulu wako! Ndi adani ako adzakugonjera; ndipo udzaponda pa misanje yao.


amene adzasanduliza thupi lathu lopepulidwa, lifanane nalo thupi lake la ulemerero, monga mwa machitidwe amene akhoza kudzigonjetsera nao zinthu zonse.


Ndipo Yehova anawapatsa mpumulo pozungulira ponse, monga mwa zonse adalumbirira makolo ao; ndipo pamaso pao sipanaime munthu mmodzi wa adani ao onse; Yehova anapereka adani ao onse m'manja mwao.