Masalimo 66:5 - Buku Lopatulika5 Idzani, muone ntchito za Mulungu; zochitira Iye ana a anthu nzoopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Idzani, muone ntchito za Mulungu; zochitira Iye ana a anthu nzoopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Bwerani mudzaone zimene Mulungu wachita, ntchito zake nzodabwitsa pakati pa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Bwerani mudzaone zimene Mulungu wachita, ntchito zanu ndi zoopsa ndithu pakati pa anthu. Onani mutuwo |