Masalimo 95:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti Yehova ndiye Mulungu wamkulu; ndi mfumu yaikulu yoposa milungu yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti Yehova ndiye Mulungu wamkulu; ndi mfumu yaikulu yoposa milungu yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pakuti Chauta ndiye Mulungu wamkulu, ndiye Mfumu yaikulu yopambana milungu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti Yehova ndi Mulungu wamkulu, mfumu yayikulu pamwamba pa milungu yonse. Onani mutuwo |