Masalimo 47:4 - Buku Lopatulika4 Atisankhira cholowa chathu, chokometsetsa cha Yakobo amene anamkonda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Atisankhira cholowa chathu, chokometsetsa cha Yakobo amene anamkonda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adatisankhulira dzikoli kuti likhale choloŵa chathu, adatipatsa ife anthu a Yakobe dziko lokomali pakuti amatikonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye anatisankhira cholowa chathu, chonyaditsa cha Yakobo, amene anamukonda. Sela Onani mutuwo |