Masalimo 47:5 - Buku Lopatulika5 Mulungu wakwera ndi mfuu, Yehova ndi liu la lipenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mulungu wakwera ndi mfuu, Yehova ndi liu la lipenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mulungu wakwera, anthu akumfuulira, Chauta wakwera, akumuimbira lipenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe, Yehova wakwera, akumuyimbira malipenga. Onani mutuwo |