1 Akorinto 15:25 - Buku Lopatulika25 Pakuti ayenera kuchita ufumu kufikira ataika adani onse pansi pa mapazi ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pakuti ayenera kuchita ufumu kufikira ataika adani onse pansi pa mapazi ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Paja Khristu ayenera kulamulira mpaka atagonjetsa adani ake onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pakuti Iye ayenera kulamulira mpaka Mulungu atayika pansi pa mapazi ake adani ake onse. Onani mutuwo |