Masalimo 18:47 - Buku Lopatulika47 Ndiye Mulungu amene andibwezerera chilango, nandigonjetsera mitundu ya anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Ndiye Mulungu amene andibwezerera chilango, nandigonjetsera mitundu ya anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Mulungu ndiye adandithandiza kuti ndilipsire, adagonjetsa anthu a mitundu ina, kuti akhale mu ulamuliro wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango, amene amagonjetsa anthu a mitundu yonse amene ali pansi pa ulamuliro wanga, Onani mutuwo |