Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 6:5 - Buku Lopatulika

Pakuti muimfa m'mosakumbukira Inu; m'mandamo adzakuyamikani ndani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti muimfa m'mosakumbukira Inu; m'mandamo adzakuyamikani ndani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu akufa sangathe kukutamandani ku manda. M'dziko la akufa ndani angathe kukuyamikani?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda?

Onani mutuwo



Masalimo 6:5
9 Mawu Ofanana  

Akufa salemekeza Yehova, kapena aliyense wakutsikira kuli chete:


Pamenepo ndinaitana dzina la Yehova; ndikuti, Yehova ndikupemphani landitsani moyo wanga.


Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo, ndipo ndidzafotokozera ntchito za Yehova.


M'mwazi mwanga muli phindu lanji, potsikira ine kudzenje? Ngati fumbi lidzayamika Inu? Ngati lidzalalikira choonadi chanu?


Bwerani, Yehova; kufikira liti? Ndipo alekeni atumiki anu.


Chilichonse dzanja lako lichipeza kuchichita, uchichite ndi mphamvu yako; pakuti mulibe ntchito ngakhale kulingirira ngakhale kudziwa, ngakhale nzeru, kumanda ulikupitako.


Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.