Masalimo 116:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo ndinaitana dzina la Yehova; ndikuti, Yehova ndikupemphani landitsani moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo ndinaitana dzina la Yehova; ndikuti, Yehova ndikupemphani landitsani moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono ndidapemphera potchula dzina la Chauta kuti, “Chauta ndikukupemphani, pulumutsani moyo wanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova: “Inu Yehova, pulumutseni!” Onani mutuwo |