Masalimo 116:3 - Buku Lopatulika3 Zingwe za imfa zinandizinga, ndi zowawa za manda zinandigwira: ndinapeza nsautso ndi chisoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Zingwe za imfa zinandizinga, ndi zowawa za manda zinandigwira: ndinapeza nsautso ndi chisoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Misampha ya imfa idandizinga, zoopsa za m'dziko la akufa zidandigwera. Ndidaona mavuto, nkugwidwa ndi nthumanzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. Onani mutuwo |