Masalimo 116:2 - Buku Lopatulika2 Popeza amanditcherera khutu lake, chifukwa chake ndidzaitanira Iye masiku anga onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Popeza amanditcherera khutu lake, chifukwa chake ndidzaitanira Iye masiku anga onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iye amatchera khutu kuti andimve, nchifukwa chake ndidzampempha nthaŵi zonse pamene ndili moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pakuti ananditchera khutu, ndidzayitana Iye masiku onse a moyo wanga. Onani mutuwo |