Masalimo 116:1 - Buku Lopatulika1 Ndimkonda, popeza Yehova amamva mau anga ndi kupemba kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndimkonda, popeza Yehova amamva mau anga ndi kupemba kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndimakonda Chauta chifukwa amamva mau anga omupemba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga; Iye amamva kulira kwanga kopempha chifundo. Onani mutuwo |