Masalimo 116:5 - Buku Lopatulika5 Yehova ngwa chifundo ndi wolungama; ndi Mulungu wathu ngwa nsoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yehova ngwa chifundo ndi wolungama; ndi Mulungu wathu ngwa nsoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chauta ndi wokoma mtima ndi wolungama. Mulungu wathu ndi wachifundo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo. Onani mutuwo |