Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 30:9 - Buku Lopatulika

9 M'mwazi mwanga muli phindu lanji, potsikira ine kudzenje? Ngati fumbi lidzayamika Inu? Ngati lidzalalikira choonadi chanu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 M'mwazi mwanga muli phindu lanji, potsikira ine kudzenje? Ngati fumbi lidzayamika Inu? Ngati lidzalalikira choonadi chanu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 “Kodi mudzapindulanji pa imfa yanga ngati nditsikira ku manda? Kodi ine nditasanduka fumbi, ndingathe kukutamandani? Kodi pamenepo ndingathe kulalika za kukhulupirika kwanu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga ngati nditsikira ku dzenje? Kodi fumbi lidzakutamandani Inu? Kodi lidzalengeza za kukhulupirika kwanu?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 30:9
7 Mawu Ofanana  

Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo, ndipo ndidzafotokozera ntchito za Yehova.


Pakuti muimfa m'mosakumbukira Inu; m'mandamo adzakuyamikani ndani?


Ndinamfuulira Iye pakamwa panga, ndipo ndinamkuza ndi lilime langa.


Chilichonse dzanja lako lichipeza kuchichita, uchichite ndi mphamvu yako; pakuti mulibe ntchito ngakhale kulingirira ngakhale kudziwa, ngakhale nzeru, kumanda ulikupitako.


Pakuti kunsi kwa manda sikungakuyamikeni Inu; imfa singakulemekezeni; Otsikira kudzenje sangaziyembekeze zoona zanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa