Masalimo 6:6 - Buku Lopatulika6 Ndalema nako kuusa moyo kwanga; ndiyandamitsa kama wanga usiku wonse; mphasa yanga ndiolobza ndi misozi yanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndalema nako kuusa moyo kwanga; ndiyandamitsa kama wanga usiku wonse; mphasa yanga ndiolobza ndi misozi yanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndatopa nkubuula kwambiri. Ndimanyowetsa bedi langa ndi misozi usiku uliwonse. Ndimakhathamiza pogona panga chifukwa cha kulira kwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ine ndatopa ndi kubuwula; usiku wonse pa bedi panga pamadzaza ndi misozi yanga; ndimanyowetsa pogona panga ndi misozi. Onani mutuwo |