Masalimo 6:7 - Buku Lopatulika7 Lapuwala diso langa chifukwa cha chisoni; lakalamba chifukwa cha onse akundisautsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Lapuwala diso langa chifukwa cha chisoni; lakalamba chifukwa cha onse akundisautsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Maso anga atupa chifukwa cha kulira, afooka chifukwa cha adani anga onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Maso anga atupa chifukwa cha chisoni; akulephera kuona chifukwa cha adani anga. Onani mutuwo |