Masalimo 6:8 - Buku Lopatulika8 Chokani kwa ine, nonsenu akuchita zopanda pake; pakuti wamva Yehova mau a kulira kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chokani kwa ine, nonsenu akuchita zopanda pake; pakuti wamva Yehova mau a kulira kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chokani apa, inu nonse ochita zoipa, Chauta wamva kulira kwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa, pakuti Yehova wamva kulira kwanga. Onani mutuwo |