Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 6:9 - Buku Lopatulika

9 Wamva Yehova kupemba kwanga; Yehova adzalandira pemphero langa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Wamva Yehova kupemba kwanga; Yehova adzalandira pemphero langa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Chauta wamva pemphero langa ndipo wandiyankha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo; Yehova walandira pemphero langa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 6:9
15 Mawu Ofanana  

popeza mtima wako unali woolowa, ndipo wadzichepetsa pamaso pa Mulungu, pakumva mau ake otsutsana nao malo ano, ndi okhala m'mwemo, ndi kudzichepetsa pamaso panga, ndi kung'amba zovala zako, ndi kulira pamaso panga; Inenso ndakumvera, ati Yehova.


M'mene ndinasautsika ndinaitanira pa Yehova; anandiyankha nandiika motakasuka Yehova.


Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza.


Tsiku loitana ine, munandiyankha, munandilimbitsa ndi mphamvu m'moyo mwanga.


Ndifuula kwa Yehova ndi mau anga, ndipo andiyankha m'phiri lake loyera.


Ndipo ine, pakutenga nkhawa, ndinati, Ndadulidwa kundichotsa pamaso panu. Komatu munamva mau a kupemba kwanga pamene ndinafuulira kwa Inu.


Ukanene kwa Hezekiya, Atero Yehova, Mulungu wa Davide, kholo lako, Ndamva kupemphera kwako, ndaona misozi yako; taona, ndidzaonjezera pa masiku ako zaka khumi ndi zisanu.


munamva mau anga; musabise khutu lanu popuma ndi pofuula ine.


Ndipo anati, Ndinaitana Yehova m'nsautso wanga, ndipo anandiyankha ine; ndinafuula ndili m'mimba ya manda, ndipo munamva mau anga.


Pokomoka moyo wanga m'kati mwanga ndinakumbukira Yehova; ndi pemphero langa linafikira Inu mu Kachisi wanu wopatulika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa