Masalimo 6:9 - Buku Lopatulika9 Wamva Yehova kupemba kwanga; Yehova adzalandira pemphero langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Wamva Yehova kupemba kwanga; Yehova adzalandira pemphero langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chauta wamva pemphero langa ndipo wandiyankha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo; Yehova walandira pemphero langa. Onani mutuwo |