Masalimo 6:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti muimfa m'mosakumbukira Inu; m'mandamo adzakuyamikani ndani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti muimfa m'mosakumbukira Inu; m'mandamo adzakuyamikani ndani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Anthu akufa sangathe kukutamandani ku manda. M'dziko la akufa ndani angathe kukuyamikani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? Onani mutuwo |