Masalimo 90:13 - Buku Lopatulika13 Bwerani, Yehova; kufikira liti? Ndipo alekeni atumiki anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Bwerani, Yehova; kufikira liti? Ndipo alekeni atumiki anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Lezani mtima, Inu Chauta. Nanga mudzatikwiyira mpaka liti? Achitireni chifundo atumiki anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Lezani mtima Inu Yehova! Kodi mudzatikwiyira mpaka liti? Achitireni chifundo atumiki anu. Onani mutuwo |