Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 121:3 - Buku Lopatulika

Sadzalola phazi lako literereke: Iye amene akusunga sadzaodzera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Sadzalola phazi lako literereke: Iye amene akusunga sadzaodzera.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Sadzalola phazi lako kuti literereke, Iye amene amakusunga sadzaodzera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.

Onani mutuwo



Masalimo 121:3
11 Mawu Ofanana  

Akapanda kumanga nyumba Yehova, akuimanga agwiritsa ntchito chabe; akapanda kusunga mzinda Yehova, mlonda adikira chabe.


Yehova adzamsunga, nadzamsunga ndi moyo, ndipo adzadalitsika padziko lapansi, ndipo musampereke ku chifuniro cha adani ake.


Koma Inu, Mulungu, mudzawatsitsira kudzenje la chionongeko. Anthu okhetsa mwazi ndi achinyengo masiku ao sadzafikira nusu; koma ine ndidzakhulupirira Inu.


Iye amene asunga moyo wathu tingafe, osalola phazi lathu literereke.


Adzakunyamula pa manja ao, ungagunde phazi lako pamwala.


kuti atchinjirize njira za chiweruzo, nadikire khwalala la opatulidwa ake.


Pompo udzayenda m'njira yako osaopa, osaphunthwa phazi lako.


pakuti Yehova adzalimbitsa mtima wako, nadzasunga phazi lako lingakodwe.


Ine Yehova ndiusunga uwo; ndidzauthirira madzi nthawi zonse; ndidzausunga usiku ndi usana, kuti angauipse.


amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa chikhulupiriro, kufikira chipulumutso chokonzeka kukavumbulutsidwa nthawi yotsiriza.


Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu.