Masalimo 121:2 - Buku Lopatulika2 Thandizo langa lidzera kwa Yehova, wakulenga kumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Thandizo langa lidzera kwa Yehova, wakulenga zakumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chithandizo changa nchochokera kwa Chauta, amene adalenga kumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi. Onani mutuwo |