Masalimo 91:12 - Buku Lopatulika12 Adzakunyamula pa manja ao, ungagunde phazi lako pamwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Adzakunyamula pa manja ao, ungagunde phazi lako pamwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adzakunyamula m'manja mwao, kuwopa kuti phazi lako lingapweteke ndi mwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 ndipo adzakunyamula ndi manja awo, kuti phazi lako lisagunde pa mwala. Onani mutuwo |