1 Samueli 2:9 - Buku Lopatulika9 Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Anthu okhulupirika Iye adzatchinjiriza moyo wao, koma anthu oipa adzazimirira mu mdima, pakuti munthu sapambana ndi mphamvu zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye adzateteza moyo wa anthu okhulupirika koma anthu oyipa adzawonongedwa mu mdima. “Pakuti munthu sapambana ndi mphamvu zake. Onani mutuwo |