Masalimo 41:2 - Buku Lopatulika2 Yehova adzamsunga, nadzamsunga ndi moyo, ndipo adzadalitsika padziko lapansi, ndipo musampereke ku chifuniro cha adani ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yehova adzamsunga, nadzamsunga ndi moyo, ndipo adzadalitsika pa dziko lapansi, ndipo musampereke ku chifuniro cha adani ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta adzamteteza ndi kumsunga ndi moyo. Adzatchedwa wodala pa dziko. Chauta sadzampereka kwa adani ake, kuti amchite zimene iwo akufuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake; Yehova adzamudalitsa iye mʼdziko ndipo sadzamupereka ku zofuna za adani ake. Onani mutuwo |