Masalimo 41:1 - Buku Lopatulika1 Wodala iye amene asamalira wosauka! Tsiku la tsoka Yehova adzampulumutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Wodala iye amene asamalira wosauka! Tsiku la tsoka Yehova adzampulumutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ngwodala munthu amene amaganizirako za amphaŵi, popeza kuti Chauta adzapulumutsa munthu wotere pa tsiku lamavuto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka; Yehova amamuwombola pa nthawi yamsautso. Onani mutuwo |