Eksodo 24:12 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anati kwa Mose, Ukwere kudza kwa Ine m'phiri muno, nukhale pompano; ndipo ndidzakupatsa magome amiyala, ndi chilamulo ndi malamulo ndawalembera kuti uwalangize.
Onani mutuwo
Ndipo Yehova anati kwa Mose, Ukwere kudza kwa Ine m'phiri muno, nukhale pompano; ndipo ndidzakupatsa magome amiyala, ndi chilamulo ndi malamulo ndawalembera kuti uwalangize.
Onani mutuwo
Chauta adauza Mose kuti, “Bwera kwa Ine kuphiri kuno, ndipo udikire konkuno. Ndidzakupatsa miyala imene ndalembapo malamulo, kuti ndiphunzitse anthu.”
Onani mutuwo
Yehova anati kwa Mose, “Bwera kwa ine ku phiri kuno, ndipo udikire konkuno. Ndidzakupatsa miyala imene ndalembapo malemba kuti ndiwaphunzitse.”
Onani mutuwo