Eksodo 31:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo atatha Iye kulankhula ndi Mose, paphiri la Sinai, anampatsa magome awiri a mboni, magome amiyala, olembedwa ndi chala cha Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo atatha Iye kulankhula ndi Mose, pa phiri la Sinai, anampatsa magome awiri a mboni, magome amiyala, olembedwa ndi chala cha Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chauta atatsiriza kulankhula ndi Mose pa phiri la Sinai lija, adampatsa Moseyo miyala iŵiri yaumboni, imene Mulungu mwini anali atalembapo kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Yehova atamaliza kuyankhula ndi Mose pa phiri la Sinai, anamupatsa Mose miyala iwiri yaumboni, imene Mulungu analembapo ndi chala chake. Onani mutuwo |