Nehemiya 9:13 - Buku Lopatulika13 Munatsikiranso paphiri la Sinai, nimunalankhula nao mochokera mu Mwamba, ndipo munawapatsa maweruzo oyenera, ndi chilamulo choona, malemba, ndi malamulo okoma; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Munatsikiranso pa phiri la Sinai, nimunalankhula nao mochokera m'Mwamba, ndipo munawapatsa maweruzo oyenera, ndi chilamulo choona, malemba, ndi malamulo okoma; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mudatsika pa phiri la Sinai, ndipo mudalankhula nawo kuchokera kumwamba. Mudaŵapatsa malangizo olungama, malamulo oona, zophunzitsa zabwino ndiponso mau aluntha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Munatsika pa Phiri la Sinai, ndipo munawayankhula kuchokera kumwamba. Munawapatsa malangizo olungama, ziphunzitso zoona ndiponso malamulo abwino. Onani mutuwo |