Masalimo 19:12 - Buku Lopatulika12 Adziwitsa zolowereza zake ndani? Mundimasule kwa zolakwa zobisika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Adziwitsa zolowereza zake ndani? Mundimasule kwa zolakwa zobisika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nanga ndani angathe kudziŵa zolakwa zake? Inu Chauta, mundichotsere zolakwa zanga zobisika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndani angathe kudziwa zolakwa zake? Mundikhululukire zolakwa zanga zobisika. Onani mutuwo |