Eksodo 24:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Mose analowa m'kati mwa mtambo, nakwera m'phirimo; ndipo Mose anakhala m'phiri masiku makumi anai usana ndi usiku. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Mose analowa m'kati mwa mtambo, nakwera m'phirimo; ndipo Mose anakhala m'phiri masiku makumi anai usana ndi usiku. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mose adakaloŵa mumtambomo mpaka kukafika pamwamba pa phiri. Adakhala kumeneko masiku makumi anai, usana ndi usiku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo Mose analowa mʼmitambo nakwera phiri. Iye anakhala ku phiriko 40 usana ndi usiku. Onani mutuwo |