Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 66:1 - Buku Lopatulika

Fuulirani kwa Mulungu, dziko lonse lapansi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Fuulirani kwa Mulungu, dziko lonse lapansi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tamandani Mulungu ndi chimwemwe mokweza mau, inu anthu onse a pa dziko lapansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Fuwulani kwa Mulungu ndi chimwemwe, dziko lonse lapansi!

Onani mutuwo



Masalimo 66:1
11 Mawu Ofanana  

Momwemo Aisraele onse anakwera nalo likasa la chipangano la Yehova ndi kufuula, ndi kumveka kwa lipenga, ndi mphalasa, ndi nsanje zomveketsa, ndi zisakasa, ndi azeze.


Fuulirani kwa Yehova, inu, dziko lonse lapansi.


Zonse zakupuma zilemekeze Yehova. Aleluya.


Kwa Iye wakuberekeka pamwambamwamba, oyambira kale lomwe; taonani; amveketsa liu lake, ndilo liu lamphamvu.


Imbitsirani Mulungu ndiye mphamvu yathu; fuulirani kwa Mulungu wa Yakobo.


Muimbireni Yehova nyimbo yatsopano; muimbireni Yehova, inu, dziko lonse lapansi.


Fuulirani kwa Yehova, inu, dziko lonse lapansi; kuwitsani ndi kufuulira mokondwera; inde, imbirani zomlemekeza.


Kuchokera ku malekezero a dziko ife tamva nyimbo zolemekeza wolungama. Koma ine ndinati, Ndaonda ine, ndaonda ine, tsoka kwa Ine! Amalonda onyenga amangonyenga; inde ogulitsa onyenga apambana kunyenga.