Masalimo 100:1 - Buku Lopatulika1 Fuulirani kwa Yehova, inu, dziko lonse lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Fuulirani kwa Yehova, inu, dziko lonse lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Fuulani kwa Chauta ndi chimwemwe, inu maiko onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi. Onani mutuwo |