Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 19:2 - Buku Lopatulika

Usana ndi usana uchulukitsa mau, ndipo usiku ndi usiku uonetsa nzeru.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Usana ndi usana uchulukitsa mau, ndipo usiku ndi usiku uonetsa nzeru.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Usana umasimbira zimenezo usana unzake, usiku umadziŵitsa zimenezo usiku unzake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri, usiku ndi usiku zimaonetsa poyera nzeru.

Onani mutuwo



Masalimo 19:2
14 Mawu Ofanana  

Ndipo anati Mulungu, Pakhale thambo pakati pamadzi, lilekanitse madzi ndi madzi.


Ndipo Mulungu anapanga thambo, nalekanitsa madzi anali pansi pathambolo ndi madzi anali pamwamba pathambolo; ndipo kunatero.


Pakukhalabe masiku a dziko lapansi, nthawi yakubzala ndi yakukunkha, chisanu ndi mafundi, malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku sizidzalekai.


Anyamata ndiponso anamwali; okalamba pamodzi ndi ana.


Aleluya. Lemekezani Mulungu m'malo ake oyera; mlemekezeni m'thambo la mphamvu yake.


Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu, munakonza kuunika ndi dzuwa.


munthu ndani kuti mumkumbukira? Ndi mwana wa munthu kuti mucheza naye?


Wamoyo, wamoyo, iye adzakuyamikani inu, monga ine lero; Atate adzadziwitsa ana ake zoona zanu.