Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 74:16 - Buku Lopatulika

16 Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu, munakonza kuunika ndi dzuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu, munakonza kuunika ndi dzuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Mudalenga usana ndi usiku. Mudaika mwezi ndi dzuŵa m'malo mwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso; Inuyo munakhazikitsa dzuwa ndi mwezi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 74:16
10 Mawu Ofanana  

Anaika mwezi nyengo zake; dzuwa lidziwa polowera pake.


Muika mdima ndipo pali usiku; pamenepo zituluka zilombo zonse za m'thengo.


Pakuona ine thambo la kumwamba lanu, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene munazikhazika,


Ine ndilenga kuyera ndi mdima, Ine ndilenga mtendere ndi choipa, Ine ndine Yehova wochita zinthu zonse zimenezi.


Yehova atero: Likaleka kukhala pangano langa la usana ndi usiku, ngati sindinalemba malemba a kumwamba ndi dziko lapansi;


kotero kuti mukakhale ana a Atate wanu wa Kumwamba; chifukwa Iye amakwezera dzuwa lake pa oipa ndi pa abwino, namavumbitsira mvula pa olungama ndi pa osalungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa