Masalimo 74:17 - Buku Lopatulika17 Munaika malekezero onse a dziko lapansi; munalenga dzinja ndi malimwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Munaika malekezero onse a dziko lapansi; munalenga dzinja ndi malimwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mudalemba malire a dziko lapansi, mudakhazikitsa chilimwe ndi dzinja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi; munakhazikitsa chilimwe ndi dzinja. Onani mutuwo |