Masalimo 74:18 - Buku Lopatulika18 Mukumbukire ichi, Yehova, mdaniyo anatonza, ndipo anthu opusa ananyoza dzina lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Mukumbukire ichi, Yehova, mdaniyo anatonza, ndipo anthu opusa ananyoza dzina lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Kumbukirani, Inu Chauta, kuti adani amakunyodolani, kuti anthu achipongwe amanyoza dzina lanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova, momwe anthu opusa apeputsira dzina lanu. Onani mutuwo |