Masalimo 74:19 - Buku Lopatulika19 Musapereke moyo wa njiwa yanu kwa chilombo; musamaiwala moyo wa ozunzika anu nthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Musapereke moyo wa njiwa yanu kwa chilombo; musamaiwala moyo wa ozunzika anu nthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Musati mupereke moyo wa nkhunda yanu Israele ku zilombo zakuthengo. Musaiŵale mpaka muyaya moyo wa anthu anu osauka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo; nthawi zonse musayiwale miyoyo ya anthu anu osautsidwa. Onani mutuwo |