Masalimo 74:20 - Buku Lopatulika20 Samalirani chipanganocho; pakuti malo a mdima a m'dziko adzala ndi zokhalamo chiwawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Samalirani chipanganocho; pakuti malo a mdima a m'dziko adzala ndi zokhalamo chiwawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Kumbukirani chipangano chanu, pakuti malo obisika am'dziko asanduka mochitira zankhanza zambirimbiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko asanduka mochitira zachiwawa zochuluka. Onani mutuwo |