Genesis 1:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo anati Mulungu, Pakhale thambo pakati pamadzi, lilekanitse madzi ndi madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo anati Mulungu, Pakhale thambo pakati pamadzi, lilekanitse madzi ndi madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kenaka Mulungu adati, “Pakhale cholekanitsa madzi, kuti madziwo akhale pa malo aŵiri olekana,” ndipo zidachitikadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka Mulungu anati, “Pakhale thambo pakati pa madzi kuti lilekanitse madzi a mʼmwamba ndi madzi a pansi.” Onani mutuwo |